1 Mbiri 3:1-24 NYCCL2016 - Bible AI

1Ana aamuna a Davide amene anabadwira ku Hebroni anali awa: Woyamba anali Amnoni, amayi ake anali Ahinoamu wa ku Yezireeli; wachiwiri anali Danieli, amayi ake anali Abigayeli wa ku Karimeli;

2wachitatu anali Abisalomu, mwana wa Maaka mwana wa Talimai mfumu ya Gesuri;

2wachinayi anali Adoniya amayi ake anali Hagiti;

3wachisanu anali Sefatiya, amayi ake anali Abitali;

3wachisanu ndi chimodzi anali Itireamu, amayi ake anali Egila.

4Ana asanu ndi mmodzi awa a Davide anabadwira ku Hebroni kumene analamulirako zaka zisanu ndi ziwiri ndi miyezi isanu ndi umodzi.

4Davide analamuliranso mu Yerusalemu kwa zaka 33,

5ndipo ana amene anabadwira ku Yerusalemuko anali awa:

5Samua, Sobabu, Natani ndi Solomoni. Ana anayi awa anali a Batisuwa mwana wa Amieli.

6Anaberekanso Ibihari, Elisua, Elipeleti,

7Noga, Nefegi, Yafiya,

8Elisama, Eliada ndi Elifeleti, onse analipo asanu ndi anayi.

9Onsewa anali ana a Davide, osawerengera ana a azikazi. Ndipo mlongo wawo anali Tamara.

9

10Mwana wa Solomoni anali Rehabiamu, Abiya anabereka Asa, Asa anabereka Yehosafati,

10Rehabiamu anabereka Abiya,

11Yehosafati anabereka Yehoramu, Ahaziya anabereka Yowasi,

11Yehoramu anabereka Ahaziya,

12Yowasi anabereka Amaziya, Azariya anabereka Yotamu,

12Amaziya anabereka Azariya,

13Yotamu anabereka Ahazi, Hezekiya anabereka Manase,

13Ahazi anabereka Hezekiya,

14Manase anabereka Amoni,

14Amoni anabereka Yosiya.

15Ana a Yosiya anali awa: Yehoyakimu mwana wake wachiwiri, Zedekiya mwana wake wachitatu, Salumu mwana wake wachinayi.

15Yohanani mwana wake woyamba,

16Ana a Yehoyakimu: ndi Zedekiya mwana wake.

16Yekoniya

17Zidzukulu za Yekoniya wa mʼndende zinali izi:

17mwana wake Silatieli,

18Malikiramu, Pedaya, Senazara, Yekamiya, Hosama ndi Nedabiya.

18

19Ana a Pedaya anali awa: Ana a Zerubabeli anali awa: Mesulamu ndi Hananiya. Mlongo wawo anali Selomiti.

19Zerubabeli ndi Simei.

20Panalinso ana ena asanu awa:

20Hasubu, Oheli, Berekiya, Hasabiya ndi Yusabu-Hesedi.

21Zidzukulu za Hananiya zinali izi:

21Pelatiya ndi Yesaiya, ndiponso ana a Refaya, ana a Arinani, ana a Obadiya ndi ana a Sekaniya.

22Zidzukulu za Sekaniya zinali izi: Hatusi, Igala, Bariya, Neariya ndi Safati. Onse anali asanu ndi mmodzi.

22Semaya ndi ana ake:

23Ana a Neariya anali awa:

23Eliyoenai, Hezekiya ndi Azirikamu. Onse anali atatu.

24Ana a Eliyoenai: Hodaviya, Eliyasibu, Pelaya, Akubu,

24Yohanani, Delaya ndi Anani, onse anali asanu ndi awiri.