1Iwe Israeli bwerera kwa Yehova Mulungu wako.Machimo anu ndi amene akugwetsani!
2Bweretsani zopempha zanundipo bwererani kwa Yehova.Munene kwa Iye kuti,“Tikhululukireni machimo athu onsendi kutilandira mokoma mtima,kuti tithe kukuyamikani ndi mawu a pakamwa pathu.
3Asiriya sangatipulumutse;ife sitidzakwera pa akavalo ankhondo,sitidzanenanso kuti, ‘Milungu yathu’kwa zimene manja athu omwe anazipanga,pakuti ndinu amene mumachitira chifundo ana amasiye.”