1Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Monga mwa mayimbidwe seminiti. Salimo la Davide.Thandizeni Yehova pakuti palibe munthu wokhulupirika;okhulupirika akusowa pakati pa anthu.
4Pakamwa pamene pamati, “Ife tidzapambana ndi kuyankhula kwathu;pakamwapa ndi pathupathu, tsono mbuye wathu ndani?”
4
5“Chifukwa cha kuponderezedwa kwa anthu opanda mphamvundi kubuwula kwa anthu osowa,Ine ndidzauka tsopano,” akutero Yehova,“Ndidzawateteza kwa owazunza.”
6Ndipo mawu a Yehova ndi angwiromonga siliva oyengedwa mʼngʼanjo yadothi,oyengedwa kasanu nʼkawiri.
6
7Inu Yehova mudzatitchinjiriza ndipomudzatiteteza kwa anthu otere kwamuyaya.