1Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe, ndakatulo ya Davide; pamene Doegi Mwedomu anapita kwa Sauli ndi kunena kuti “Davide wapita ku nyumba ya Ahimeleki.”Nʼchifukwa chiyani ukudzitamandira ndi zoyipa, iwe munthu wamphamvu?Nʼchifukwa chiyani ukudzitamandira tsiku lonse,iwe munthu wochititsa manyazi pamaso pa Mulungu?
2Tsiku lonse umakhalira kuganizira za kuwononga ena;lilime lako lili ngati lumo lakuthwa,ntchito yako nʼkunyenga.